1 Mbiri 6:3-12
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
3 Ana a Amramu anali awa:
Aaroni, Mose ndi Miriamu.
Ana a Aaroni anali awa:
Nadabu, Abihu, Eliezara ndi Itamara
4 Eliezara anabereka Finehasi,
Finehasi anabereka Abisuwa,
5 Abisuwa anabereka Buki,
Buki anabereka Uzi.
6 Uzi anabereka Zerahiya,
Zerahiya anabereka Merayoti,
7 Merayoti anabereka Amariya,
Amariya anabereka Ahitubi.
8 Ahitubi anabereka Zadoki,
Zadoki anabereka Ahimaazi.
9 Ahimaazi anabereka Azariya,
Azariya anabereka Yohanani,
10 Yohanani anabereka Azariya (uyu ndi amene anatumikira monga wansembe mʼNyumba ya Mulungu imene Solomoni anamanga mu Yerusalemu),
11 Azariya anabereka Amariya,
Amariya anabereka Ahitubi,
12 Ahitubi anabereka Zadoki,
Zadoki anabereka Salumu,
The Word of God in Contemporary Chichewa Copyright © 2002, 2016 by Biblica, Inc.® Used by permission of Biblica, Inc.® All rights reserved worldwide. Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero Mwini © 2002, 2016 ndi Biblica, Inc.® Kugwiritsa ntchito mwachilolezo. Umwini ndi otetezedwa pa dziko lonse.