Add parallel Print Page Options

Abwenzi

13 Bwerera, bwerera iwe namwali wa ku Sulami;
    bwerera, bwerera kuti ife tidzakupenyetsetse iwe!

Mwamuna

Chifukwa chiyani mukufuna kudzapenyetsetsa ine mwana wamkazi wa ku Sulami,
    pamene ndikuvina pakati pa magulu awiri?

Read full chapter