Font Size
Luka 24:44
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
Luka 24:44
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
44 Iye anawawuza kuti, “Izi ndi zimene ndinakuwuzani pamene ndinali nanu: chilichonse chiyenera kukwaniritsidwa chimene chinalembedwa cha Ine mʼbuku la Malamulo a Mose, Aneneri ndi Masalimo.”
Read full chapter
Luka 24:45
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
Luka 24:45
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
45 Kenaka anawatsekula maganizo kuti azindikire Malemba.
Read full chapter
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (CCL)
The Word of God in Contemporary Chichewa Copyright © 2002, 2016 by Biblica, Inc.® Used by permission of Biblica, Inc.® All rights reserved worldwide. Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero Mwini © 2002, 2016 ndi Biblica, Inc.® Kugwiritsa ntchito mwachilolezo. Umwini ndi otetezedwa pa dziko lonse.