Psalm 108:5-7
Christian Standard Bible
5 God, be exalted above the heavens,(A)
and let your glory be over the whole earth.(B)
6 Save with your right hand and answer me
so that those you love may be rescued.(C)
7 God has spoken in his sanctuary:[a]
“I will celebrate!
I will divide up Shechem.(D)
I will apportion the Valley of Succoth.(E)
Footnotes
- 108:7 Or has promised by his holy nature
Masalimo 108:5-7
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
5 Kwezekani Inu Mulungu, kuposa mayiko akumwamba,
ndipo ulemerero wanu uphimbe dziko lonse lapansi.
6 Tipulumutseni ndi kutithandiza ndi dzanja lanu lamanja
kuti iwo amene mumawakonda apulumutsidwe.
7 Mulungu wayankhula kuchokera ku malo ake opatulika:
“Mwachipambano Ine ndidzagawa Sekemu
ndipo ndidzayesa chigwa cha Sukoti.
The Christian Standard Bible. Copyright © 2017 by Holman Bible Publishers. Used by permission. Christian Standard Bible®, and CSB® are federally registered trademarks of Holman Bible Publishers, all rights reserved.
The Word of God in Contemporary Chichewa Copyright © 2002, 2016 by Biblica, Inc.® Used by permission of Biblica, Inc.® All rights reserved worldwide. Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero Mwini © 2002, 2016 ndi Biblica, Inc.® Kugwiritsa ntchito mwachilolezo. Umwini ndi otetezedwa pa dziko lonse.