God, be exalted above the heavens,(A)
and let your glory be over the whole earth.(B)
Save with your right hand and answer me
so that those you love may be rescued.(C)

God has spoken in his sanctuary:[a]
“I will celebrate!
I will divide up Shechem.(D)
I will apportion the Valley of Succoth.(E)

Read full chapter

Footnotes

  1. 108:7 Or has promised by his holy nature

Kwezekani Inu Mulungu, kuposa mayiko akumwamba,
    ndipo ulemerero wanu uphimbe dziko lonse lapansi.

Tipulumutseni ndi kutithandiza ndi dzanja lanu lamanja
    kuti iwo amene mumawakonda apulumutsidwe.
Mulungu wayankhula kuchokera ku malo ake opatulika:
    “Mwachipambano Ine ndidzagawa Sekemu
    ndipo ndidzayesa chigwa cha Sukoti.

Read full chapter