Font Size
Nyimbo ya Solomoni 6:13
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
Nyimbo ya Solomoni 6:13
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
Abwenzi
13 Bwerera, bwerera iwe namwali wa ku Sulami;
bwerera, bwerera kuti ife tidzakupenyetsetse iwe!
Mwamuna
Chifukwa chiyani mukufuna kudzapenyetsetsa ine mwana wamkazi wa ku Sulami,
pamene ndikuvina pakati pa magulu awiri?
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (CCL)
The Word of God in Contemporary Chichewa Copyright © 2002, 2016 by Biblica, Inc.® Used by permission of Biblica, Inc.® All rights reserved worldwide. Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero Mwini © 2002, 2016 ndi Biblica, Inc.® Kugwiritsa ntchito mwachilolezo. Umwini ndi otetezedwa pa dziko lonse.